Numeri 35:24 - Buku Lopatulika24 pamenepo msonkhano uziweruza pakati pa wokantha mnzakeyo ndi wolipsa mwaziyo monga mwa maweruzo awa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 pamenepo msonkhano uziweruza pakati pa wokantha mnzakeyo ndi wolipsa mwaziyo monga mwa maweruzo awa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 pamenepo mpingo uweruze pakati pa munthu wopha mnzakeyo ndi mbale wa munthu wakufayo, potsata malangizo ameneŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 gulu liweruze pakati pa iye ndi wolipsira monga mwa malamulo ake. Onani mutuwo |