Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 35:23 - Buku Lopatulika

23 kapena kumponyera mwala wakufetsa munthu, osamuona, namgwetsera uwu, kuti wafa, koma sindiye mdani wake, kapena womfunira choipa;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 kapena kumponyera mwala wakufetsa munthu, osamuona, namgwetsera uwu, kuti wafa, koma sindiye mdani wake, kapena womfunira choipa;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 kapena amulasa ndi mwala woti nkupha munthu, koma amlasa osamuwona mnzakeyo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 kapena mosamuona nʼkumuponyera mwala womwe utha kumupha, munthuyo nʼkufa, tsono pakuti sanali mdani wake ndipo sanaganizire zomupweteka,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 35:23
2 Mawu Ofanana  

Koma akampyoza modzidzimuka, osamuda, kapena kumponyera kanthu osamlalira,


pamenepo msonkhano uziweruza pakati pa wokantha mnzakeyo ndi wolipsa mwaziyo monga mwa maweruzo awa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa