Numeri 35:22 - Buku Lopatulika22 Koma akampyoza modzidzimuka, osamuda, kapena kumponyera kanthu osamlalira, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma akampyoza modzidzimuka, osamuda, kapena kumponyera kanthu osamlalira, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 “Koma ngati munthu abaya mnzake mwangozi osati chifukwa cha chidani, kapena alasa mnzake ndi chida osamubisalira, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “ ‘Koma ngati popanda udani wina uliwonse, mwadzidzidzi akankha wina kapena kumuponyera chinthu osati mwadala, Onani mutuwo |