Numeri 35:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo akampyoza momkwiyira, kapena kumponyera kanthu momlalira, kuti wafa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo akampyoza momkwiyira, kapena kumponyera kanthu momlalira, kuti wafa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ndipo ngati munthu abaya mnzake chifukwa cha chidani, kapena amulasa ndi chida atamubisalira, mnzakeyo naafa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ndipo ngati wina wake, chifukwa cha udani, aganiza zokankha munthu wina kapena kumuponyera chinthu china mwadala munthuyo nʼkufa, Onani mutuwo |