Numeri 35:19 - Buku Lopatulika19 Wolipsa mwazi mwini wake aphe wakupha munthuyo; pakumpeza amuphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Wolipsa mwazi mwini wake aphe wakupha munthuyo; pakumpeza amuphe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mbale wake wa munthu wakufayo ndiye adzaphe wopha mnzakeyo. Akadzangokumana, wopha mnzakeyo adzamuphe ndi munthu wolipsira magaziyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Wolipsira adzamuphanso wakuphayo. Pamene akumana naye adzayenera kumupha ndithu. Onani mutuwo |
Ndipo onani, chibale chonse chinaukira mdzakazi wanu, ndi kuti, Upereke iye amene anakantha mbale wake, kuti timuphe chifukwa cha moyo wa mbale wake amene anamupha; koma pakutero adzaononga wolowa yemwe; chomwecho adzazima khala langa lotsala, ndipo sadzasiyira mwamuna wanga dzina kapena mbeu kunja kuno.