Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 35:14 - Buku Lopatulika

14 Mupereke mizinda itatu tsidya lino la Yordani, ndi mizinda itatu mupereke m'dziko la Kanani, ndiyo yopulumukirako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Mupereke midzi itatu tsidya lino la Yordani, ndi midzi itatu mupereke m'dziko la Kanani, ndiyo yopulumukirako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Mudzapereke mizinda itatu patsidya la kuvuma la mtsinje wa Yordani, ndi mizinda itatu m'dziko la Kanani, kuti ikhale mizinda yothaŵirako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Mupereke itatu mbali ino ya Yorodani ndi itatu ina mu Kanaani kuti ikhale mizinda yopulumukirako.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 35:14
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mizindayo muipereke ikukhalireni mizinda isanu ndi umodzi yopulumukirako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa