Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 33:37 - Buku Lopatulika

37 Nachokera ku Kadesi, nayenda namanga m'phiri la Hori, ku malekezero a dziko la Edomu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Nachokera ku Kadesi, nayenda namanga m'phiri la Hori, ku malekezero a dziko la Edomu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Adanyamuka ku Kadesi, nakamanga mahema ao ku phiri la Hori m'mbali mwa dziko la Edomu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Anachoka ku Kadesi ndi kukamanga ku phiri la Hori, mʼmalire mwa dziko la Edomu.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:37
3 Mawu Ofanana  

Pamenepo tinafuulira kwa Yehova, ndipo anamva mau athu, natuma mthenga, natitulutsa mu Ejipito; ndipo, taonani, tili mu Kadesi, ndiwo mzinda wa malekezero a malire anu.


Ndipo anayenda ulendo kuchokera kuphiri la Hori, nadzera njira ya Nyanja Yofiira, kupaza ku dziko la Edomu; ndi mtima wa anthu unada chifukwa cha njirayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa