Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:48 - Buku Lopatulika

48 Pamenepo akazembe a pa ankhondo zikwi, atsogoleri a zikwi, ndi atsogoleri a mazana, anayandikiza kwa Mose;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Pamenepo akazembe a pa ankhondo zikwi, atsogoleri a zikwi, ndi atsogoleri a mazana, anayandikiza kwa Mose;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Pamenepo akulu a nkhondo amene ankayang'anira ankhondo onse, ndiye kuti atsogoleri olamulira ankhondo zikwi, ndi atsogoleri olamulira ankhondo mazana, adabwera kwa Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Pamenepo omwe ankayangʼanira magulu a ankhondo olamulira 1,000 ndi olamulira 100 anabwera kwa Mose,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:48
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anakwiya nao akazembe a nkhondoyi, atsogoleri a zikwi, atsogoleri a mazana, akufuma kunkhondo adaithira.


mwa gawolo la ana a Israele Mose anatenga munthu mmodzi mwa makumi asanu, ndi zoweta momwemo, nazipereka kwa Alevi, akusunga udikiro wa chihema cha Yehova; monga Yehova adamuuza Mose.


nati kwa Mose, Atumiki anu anawerenga ankhondo tinali nao, ndipo sanasowe munthu mmodzi wa ife.


Ndipo akapitao anene ndi anthu, ndi kuti, Ndani munthuyo anamanga nyumba yatsopano, osalowamo? Amuke nabwerere kunyumba kwake, kuti angafe kunkhondo nangalowemo munthu wina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa