Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 31:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo ng'ombe zidafikira zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi awiri mphambu ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo ng'ombe zidafikira zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi chimodzi; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi awiri mphambu ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Ng'ombe zinalipo 36,000, ndipo 72 zinali gawo la Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 ngʼombe zinalipo 36,000 ndipo gawo la Yehova linali 72;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:38
3 Mawu Ofanana  

Ndi pamodzi nao mwa mibadwo yao, mwa nyumba za makolo ao, panali magulu a nkhondo zikwi makumi atatu mphambu zisanu ndi chimodzi, popeza anachuluka akazi ao ndi ana ao.


Ndi msonkho wa Yehova wankhosa ndiwo mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu.


Ndipo abulu anafikira zikwi makumi atatu ndi mazana asanu; pamenepo msonkho wa Yehova ndiwo makumi asanu ndi limodzi mphambu mmodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa