Numeri 29:20 - Buku Lopatulika20 Ndi tsiku lachitatu ng'ombe khumi ndi imodzi, nkhosa zamphongo ziwiri, anaankhosa khumi ndi anai a chaka chimodzi opanda chilema; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndi tsiku lachitatu ng'ombe khumi ndi imodzi, nkhosa zamphongo ziwiri, anaankhosa khumi ndi anai a chaka chimodzi opanda chilema; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Pa tsiku lachitatu mupereke ng'ombe zamphongo khumi ndi imodzi, nkhosa ziŵiri zamphongo, anaankhosa khumi ndi anai amphongo, a chaka chimodzi, opanda chilema, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 “ ‘Pa tsiku lachitatu muzipereka ngʼombe zazimuna khumi ndi imodzi, nkhosa zazimuna ziwiri ndi ana ankhosa aamuna khumi ndi anayi a chaka chimodzi, zonse zopanda chilema. Onani mutuwo |