Nehemiya 9:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo lichulukitsira mafumu zipatso zake, ndiwo amene munawaika atiweruze, chifukwa cha zoipa zathu; achitanso ufumu pa matupi athu, ndi pa zoweta zathu, monga umo akonda; ndipo ife tisauka kwakukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo lichulukitsira mafumu zipatso zake, ndiwo amene munawaika atiweruze, chifukwa cha zoipa zathu; achitanso ufumu pa matupi athu, ndi pa zoweta zathu, monga umo akonda; ndipo ife tisauka kwakukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsopano chuma cha dzikolo changolemeza mafumu amene mudaŵaika kuti azitilamulira kaamba ka machimo athu. Ali ndi mphamvu zolamulira matupi athu ndiponso ng'ombe zathu monga afunira. Ndithudi, ife tili m'mavuto aakulu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Tsono chifukwa cha machimo athu, mafumu amene munawayika kuti azitilamulira angodzilemeretsa ndi chuma chambiri cha dzikoli. Iwo ali ndi mphamvu zolamulira matupi athu ndi ngʼombe zathu momwe afunira. Zedi, ife tili mʼmavuto aakulu.” Onani mutuwo |