Nehemiya 9:36 - Buku Lopatulika36 Tapenyani, ife lero ndife akapolo, ndi dzikoli mudalipereka kwa makolo athu kudya zipatso zake ndi zokoma zake, taonani, ife ndife akapolo m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Tapenyani, ife lero ndife akapolo, ndi dzikoli mudalipereka kwa makolo athu kudya zipatso zake ndi zokoma zake, taonani, ife ndife akapolo m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Onani, ife ndife akapolo lero lino, ndife akapolo m'dziko limene mudapatsa makolo athu, kuti azidya zipatso zake ndi zabwino zake zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 “Tsono, taonani! Ife lero ndife akapolo, ndife akapolo mʼdziko limene munapereka kwa makolo athu kuti azidya zipatso zake ndi zabwino zake zonse. Onani mutuwo |