Nehemiya 9:35 - Buku Lopatulika35 Popeza sanatumikire Inu mu ufumu wao, ndi mu ubwino wanu wochuluka umene mudawapatsa, ndi m'dziko lalikulu ndi la zonona mudalipereka pamaso pao, ndipo sanabwerere kuleka ntchito zao zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Popeza sanatumikire Inu m'ufumu wao, ndi m'ubwino wanu wochuluka umene mudawapatsa, ndi m'dziko lalikulu ndi la zonona mudalipereka pamaso pao, ndipo sanabwerere kuleka ntchito zao zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Pamene iwo ankadzilamulira okha, namalandira zabwino zanu m'dziko lalikulu ndi lachonde limene mudaŵapatsa, sadakutumikireni, ndipo sadazisiye ntchito zao zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Ngakhale ankadzilamulira okha, nʼkumalandira zabwino zochuluka mʼdziko lalikulu ndi lachonde limene munawapatsa, koma iwo sanakutumikireni kapena kusiya ntchito zawo zoyipa. Onani mutuwo |