Nehemiya 7:46 - Buku Lopatulika46 Antchito a m'kachisi: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Anetini: ana a Ziha, ana a Hasufa, ana a Tabaoti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Antchito a ku Nyumba ya Mulungu anali aŵa: a banja la Ziha, a banja la Hasufa, a banja la Tabaoti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti, Onani mutuwo |