Nehemiya 6:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo linga linatsirizika pa tsiku la makumi awiri ndi lachisanu la mwezi wa Eluli, titalimanga masiku makumi asanu mphambu awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo linga linatsirizika pa tsiku la makumi awiri ndi lachisanu la mwezi wa Eluli, titalimanga masiku makumi asanu mphambu awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Patapita masiku 52, pa tsiku la 25 la mwezi wa Eluli, khoma lija adatsiriza kumanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo khoma linatsirizidwa kumanga pa tsiku la 25 la mwezi wa Eluli. Linamangidwa pa masiku okwana 52. Onani mutuwo |