Nehemiya 13:31 - Buku Lopatulika31 ndi chopereka cha nkhuni pa nthawi zoikika, ndi wa zipatso zoyamba. Mundikumbukire, Mulungu wanga, chindikomere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 ndi chopereka cha nkhuni pa nthawi zoikika, ndi wa zipatso zoyamba. Mundikumbukire, Mulungu wanga, chindikomere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Chinanso, ndidalamula kuti nkhuni ndi zipatso zoyamba kucha azipereke pa nthaŵi yoyenera. Inu Mulungu wanga, mukumbukire zonsezi ndipo mundikomere mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ndiponso kupereka nkhuni ndi zipatso zoyamba kucha pa nthawi yake. Ndikumbukireni pondikomera mtima, Inu Mulungu wanga. Onani mutuwo |