Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Nehemiya 12:42 - Buku Lopatulika

42 ndi Maaseiya, ndi Semaya, ndi Eleazara, ndi Uzi, ndi Yehohanani, ndi Malikiya, ndi Elamu, ndi Ezere. Ndipo oimbira anaimbitsa Yezeraya ndiye woyang'anira wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

42 ndi Maaseiya, ndi Semaya, ndi Eleazara, ndi Uzi, ndi Yehohanani, ndi Malikiya, ndi Elamu, ndi Ezere. Ndipo oimbira anaimbitsa Yezeraya ndiye woyang'anira wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

42 Panalinso ansembe aŵa: Maaseiya, Semaya, Eleazara, Uzi, Yehohanani, Malikiya, Elamu ndi Ezero. Yezeraya ndiye ankatsogolera oimba nyimbo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

42 Panalinso ansembe awa: Maaseya, Semaya, Eliezara, Uzi, Yehohanani, Milikiya, Elamu ndi Ezeri. Gulu loyimba linkatsogozedwa ndi Yezirahayiya.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 12:42
11 Mawu Ofanana  

mwana wa Mikaele, mwana wa Baaseiya, mwana wa Malikiya,


Maaziya, Biligai, Semaya, ndiwo ansembe.


ndi abale ao, ngwazi zamphamvu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu; ndi woyang'anira wao ndiye Zabidiele mwana wa Hagedolimu.


ndi ansembe, Eliyakimu, Maaseiya, Miniyamini, Mikaya, Eliyoenai, Zekariya, ndi Hananiya, ali nao malipenga;


Ndipo anaphera nsembe zambiri tsiku lija, nasekerera; pakuti Mulungu anawakondweretsa ndi chimwemwe chachikulu; ndi akazi omwe ndi ana anakondwera; ndi chikondwerero cha Yerusalemu chinamveka kutali.


Imbitsirani Mulungu ndiye mphamvu yathu; fuulirani kwa Mulungu wa Yakobo.


Utsani salimo, bwera nakoni kalingaka, zeze wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa.


Tiyeni tiimbire Yehova mokondwera; tifuule kwa thanthwe la chipulumutso chathu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa