Nehemiya 12:40 - Buku Lopatulika40 Atatero, magulu awiriwo a iwo oyamikira anaima m'nyumba ya Mulungu, ndipo ine ndi limodzi la magawo awiri a olamulira pamodzi ndi ine; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Atatero, magulu awiriwo a iwo oyamikira anaima m'nyumba ya Mulungu, ndipo ine ndi limodzi la magawo awiri a olamulira pamodzi ndi ine; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Choncho magulu othokoza aŵiri onsewo adakaimirira pafupi ndi Nyumba ya Mulungu. Pamodzi ndi ine ndi theka la akuluakulu aja, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Choncho magulu onse awiri oyimba nyimbo zothokoza aja anakayima pafupi ndi Nyumba ya Mulungu. Pamodzi ndi ine ndi theka la atsogoleri aja, Onani mutuwo |