Nehemiya 12:39 - Buku Lopatulika39 ndi pamwamba pa Chipata cha Efuremu, ndi ku Chipata Chakale, ndi ku Chipata cha Nsomba, ndi Nsanja ya Hananele, ndi Nsanja ya Zana, mpaka ku Chipata cha Nkhosa; ndipo anaima ku Chipata cha Akaidi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 ndi pamwamba pa Chipata cha Efuremu, ndi ku Chipata Chakale, ndi ku Chipata Chansomba, ndi Nsanja ya Hananele, ndi Nsanja ya Zana, mpaka kuchipata chankhosa; ndipo anaima ku Chipata cha Akaidi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Tidadzeranso pa Chipata cha Efuremu, pa Chipata Chakale, pa Chipata cha Nsomba, pa Nsanja ya Hananele, pa Nsanja ya Zana, mpaka kukafika ku Chipata cha Nkhosa. Ndipo potsiriza tidakaima ku Chipata cha Mlonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Tinadutsanso Chipata cha Efereimu, Chipata cha Yesana, Chipata cha Nsomba, Nsanja ya Hananeli, Nsanja ya Zana mpaka kukafika ku Chipata cha Nkhosa. Ndipo mdipiti uwu unakayima pa Chipata cha Mlonda. Onani mutuwo |