Nehemiya 12:29 - Buku Lopatulika29 ndi ku Betegiligala, ndi ku minda ya Geba ndi Azimaveti; popeza oimbirawo adadzimangira midzi pozungulira Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 ndi ku Betegiligala, ndi ku minda ya Geba ndi Azimaveti; popeza oimbirawo adadzimangira midzi pozungulira Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Kudabwera enanso ochokera ku Betegiligala, ku Geba, ndi ku Azimaveti, pakuti oimba nyimbo anali atamanga midzi yao pozungulira Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Beti-Giligala ndi ku madera a ku Geba ndi Azimaveti, pakuti oyimbawo anali atamanga midzi yawo mozungulira Yerusalemu. Onani mutuwo |