Nehemiya 12:28 - Buku Lopatulika28 Ana a oimbirawo anasonkhana ochokera ku dziko lozungulira Yerusalemu, ndi kumidzi ya Anetofa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ana a oimbirawo anasonkhana ochokera ku dziko lozungulira Yerusalemu, ndi kumidzi ya Anetofa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Tsono anthu a m'mabanja a Levi oimba nyimbo, adasonkhana pamodzi, kuchokera ku malo onse ozungulira Yerusalemu, ndiponso ku midzi ya Anetofati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Tsono anthu a mabanja a Alevi oyimba nyimbo aja anasonkhana pamodzi kuchokera ku madera onse ozungulira Yerusalemu ndiponso ku midzi ya Anetofati, Onani mutuwo |