Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Nehemiya 11:35 - Buku Lopatulika

35 Lodi, ndi Ono, chigwa cha amisiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Lodi, ndi Ono, chigwa cha amisiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Lodi, Ono, ndiponso ku chigwa cha anthu aluso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 ku Lodi, Ono ndi ku chigwa cha Amisiri.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 11:35
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Meonotai anabala Ofura; ndi Seraya anabala Yowabu atate wa Geharasimu; popeza iwo ndiwo amisiri.


Ndi ana a Elipaala: Eberi, ndi Misamu, ndi Semedi, amene anamanga Ono, ndi Lodi ndi midzi yake,


Hadidi, Zeboimu, Nebalati,


Ndi magawo a Levi anakhala ena ku Yuda, ndi ena ku Benjamini.


anatumiza mau kwa ine Sanibalati ndi Gesemu, kuti, Tiyeni tikomane kumidzi ya ku Chigwa cha Ono; koma analingirira za kundichitira choipa.


Ana a Lodi, Hadidi, ndi Ono, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi awiri kudza mmodzi.


Koma kunali, pakupita Petro ponseponse, anatsikiranso kwa oyera mtima akukhala ku Lida.


Ndipo anamuona iye onse akukhala ku Lida ndi ku Saroni, natembenukira kwa Ambuye amenewa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa