Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 11:32 - Buku Lopatulika

32 pa Anatoti, Nobi, Ananiya,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 pa Anatoti, Nobi, Ananiya,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Anatoti, Nobi, Ananiya,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 ku Anatoti, Nobu ndi Ananiya,

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 11:32
10 Mawu Ofanana  

Ana a Benjamini omwe, kuyambira ku Geba pa Mikimasi, ndi Aya, ndi pa Betele ndi midzi yake,


Hazori, Rama, Gitaimu,


Amuna a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Fuula ndi mau ako iwe mwana wamkazi wa Galimu! Tamva, iwe Laisa! Iwe Anatoti wosauka!


Lero lomwe adzaima pa Nobu; agwedezera dzanja lake paphiri la mwana wamkazi wa Ziyoni, phiri la Yerusalemu.


Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini;


Anatoti ndi mabusa ake, ndi Alimoni ndi mabusa ake; mizinda inai.


Ndipo Davide anafika ku Nobu kwa Ahimeleki wansembeyo; ndipo Ahimeleki anadza kukomana ndi Davide alikunjenjemera, nanena naye, Muli nokha bwanji, palibe munthu wina nanu?


Nati Davide kwa Ahimeleki wansembeyo, Mfumu inandilamulira ntchito, ninena nane, Asadziwe munthu aliyense kanthu za ntchito imene ndakutumira ndi kukulamulira; ndipo ndawapanga anyamatawo ku malo akuti.


Ndipo anakantha Nobu ndiwo mzinda wa ansembe ndi lupanga lakuthwa, anthu aamuna ndi aakazi, ana ndi makanda, ng'ombe ndi abulu, ndi nkhosa, ndi lupanga lakuthwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa