Nahumu 3:3 - Buku Lopatulika3 munthu wokwera pa kavalo, ndi lupanga lonyezimira, ndi mkondo wong'anipa; ndi aunyinji ophedwa, ndi chimulu cha mitembo, palibe kutha zitanda; angokhumudwa ndi zitanda; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 munthu wokwera pa kavalo, ndi lupanga lonyezimira, ndi mkondo wong'anipa; ndi aunyinji ophedwa, ndi chimulu cha mitembo, palibe kutha zitanda; angokhumudwa ndi zitanda; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Okwera pa akavalo akuthamanga, malupanga ali ŵaliŵali, mikondo ili phuliphuli. Afa anthu ambiri, mitembo yati vuu, yosaŵerengeka, anthu kumaphunthwa pa mitemboyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kuthamanga kwa anthu okwera pa akavalo, kungʼanima kwa malupanga ndi kunyezimira kwa mikondo! Anthu ambiri ophedwa, milumilu ya anthu akufa, mitembo yosawerengeka, anthu akupunthwa pa mitemboyo. Onani mutuwo |