Nahumu 3:1 - Buku Lopatulika1 Tsoka mzinda wa mwazi! Udzala nao mabodza ndi zachifwamba; zachifwamba sizidukiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tsoka mudzi wa mwazi! Udzala nao mabodza ndi zachifwamba; zachifwamba sizidukiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsoka kwa mzinda wokhetsa magazi a anthu ambiri, mzinda wodzaza ndi mabodza ndi zakuba, wokonda kufunkha mosalekeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsoka kwa mzinda wopha anthu, mzinda wodzaza ndi mabodza, mzinda wodzaza ndi anthu olanda zinthu anzawo, mu mzinda mʼmene simusowa anthu osautsidwa nthawi zonse! Onani mutuwo |