Nahumu 2:7 - Buku Lopatulika7 Chatsimikizika, avulidwa, atengedwa, adzakazi ake alira ngati mau a nkhunda, nadziguguda pachifuwa pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chatsimikizika, avulidwa, atengedwa, adzakazi ake alira ngati mau a nkhunda, nadziguguda pachifuwa pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mfumukazi yake yatengedwa ukapolo. Adzakazi ake akulira ngati nkhunda, ndipo akudzigunda pa chifuwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Zatsimikizika kuti mzinda utengedwa ndi kupita ku ukapolo. Akapolo aakazi akulira ngati nkhunda ndipo akudziguguda pachifuwa. Onani mutuwo |