Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Nahumu 2:6 - Buku Lopatulika

6 Pa zipata za mitsinje patseguka, ndi chinyumba chasungunuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Pa zipata za mitsinje patseguka, ndi chinyumba chasungunuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Akutsekula zipata zotchinga dziŵe la madzi, kunyumba kwa mfumu kwadzaza mantha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Atsekula zipata zotchinga madzi a mu mtsinje ndipo nyumba yaufumu yagwa.

Onani mutuwo Koperani




Nahumu 2:6
5 Mawu Ofanana  

Akumbukira omveka ake; akhumudwa m'kupita kwao, afulumira kulinga lake, ndi chotchinjiriza chakonzeka.


Chatsimikizika, avulidwa, atengedwa, adzakazi ake alira ngati mau a nkhunda, nadziguguda pachifuwa pao.


Taona, anthu ako m'kati mwako akunga akazi, zipata za dziko lako zatsegulidwira adani ako papakulu; moto watha mipingiridzo yako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa