Nahumu 2:5 - Buku Lopatulika5 Akumbukira omveka ake; akhumudwa m'kupita kwao, afulumira kulinga lake, ndi chotchinjiriza chakonzeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Akumbukira omveka ake; akhumudwa m'kupita kwao, afulumira kulinga lake, ndi chotchinjiriza chakonzeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Atsogoleri a ankhondo akuitanidwa, akubwera naphunthwa. Akuthamangira ku linga la mzinda, akuimika chipupa chodzitetezera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye akuyitanitsa asilikali ake wolemekezeka, koma iwo akubwera napunthwa. Akuthamangira ku linga la mzinda; akuyimika chodzitchinjirizira pamalo pake. Onani mutuwo |