Nahumu 2:3 - Buku Lopatulika3 Zikopa za amphamvu ake zasanduka zofiira, ngwazi zivala mlangali; magaleta anyezimira ndi chitsulo tsiku la kukonzera kwake, ndi mikondo itinthidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Zikopa za amphamvu ake zasanduka zofiira, ngwazi zivala mlangali; magaleta anyezimira ndi chitsulo tsiku la kukonzera kwake, ndi mikondo itinthidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Zishango za ankhondo ao nzofiira, asilikali ao onse avala zovala zamlangali. Atandanda pa mizere yankhondo, magaleta ao akuchezimira ngati malaŵi a moto. Akavalo akungoti jodojodo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Zishango za ankhondo ake ndi zofiira; asilikali ake avala zovala zofiirira. Zitsulo za pa magaleta zikunyezimira tsiku la kukonzekera kwake. Akuonetsa mikondo ya mkungudza yonoledwa. Onani mutuwo |