Nahumu 2:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti Yehova abwezeranso ukulu wake wa Yakobo ngati ukulu wake wa Israele; pakuti okhuthula anawakhuthula, naipsa nthambi zake za mpesa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti Yehova abwezeranso ukulu wake wa Yakobo ngati ukulu wake wa Israele; pakuti okhuthula anawakhuthula, naipsa nthambi zake za mpesa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Patsala pang'ono kuti Chauta abwezere ulemerero wa Israele, monga udaaliri kale, ofunkha asanalande zinthu zonse ndi kuwononga mphesa zao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova adzabwezeretsa ulemerero wa Yakobo ngati ulemerero wa Israeli, ngakhale anthu owononga anawawononga kotheratu ndipo anawononganso mpesa wawo. Onani mutuwo |