Nahumu 1:4 - Buku Lopatulika4 Adzudzula nyanja, naiphwetsa, naumitsa mitsinje yonse; Basani ndi Karimele afota, ndi duwa la ku Lebanoni linyala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Adzudzula nyanja, naiphwetsa, naumitsa mitsinje yonse; Basani ndi Karimele afota, ndi duwa la ku Lebanoni linyala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Akangoilamula nyanja, imauma, amaumitsanso mitsinje yonse. Zomera za ku Basani ndi za ku Karimele zimauma, maluŵa a ku Lebanoni amafota. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Amalamulira nyanja ndipo imawuma; amawumitsa mitsinje yonse. Zomera za ku Basani ndi Karimeli zimawuma ndipo maluwa a ku Lebanoni amafota. Onani mutuwo |