Nahumu 1:12 - Buku Lopatulika12 Atero Yehova: Angakhale iwo ali ndi mphamvu yokwanira, nachuluka momwemo, koma momwemonso adzasalikidwa, ndipo iye adzapitiratu. Chinkana ndakuzunza iwe, sindidzakuzunzanso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Atero Yehova: Angakhale iwo ali ndi mphamvu yokwanira, nachuluka momwemo, koma momwemonso adzasalikidwa, ndipo iye adzapitiratu. Chinkana ndakuzunza iwe, sindidzakuzunzanso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Zimene akunena Chauta ndi izi, akuti, “Ngakhale Aasiriyawo ndi amphamvu ndiponso ndi ambiri, adzaonongeka ndi kutheratu. Koma inu anthu anga, ngakhale ndidakulangani, sindidzakulanganinso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yehova akuti, “Ngakhale Asiriyawo ali ndi abwenzi, kaya iwowo ndi ambiri, koma adzawonongedwa ndi kutheratu. Ngakhale ndinakuzunza iwe Yuda, sindidzakuzunzanso. Onani mutuwo |