Nahumu 1:1 - Buku Lopatulika1 Katundu wa Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Katundu wa Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Uwu ndi uthenga wonena za mzinda wa Ninive. Uthengawu ukufotokoza za zimene Nahumu wa ku Elikosi adaziwona m'masomphenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uthenga wonena za Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi. Onani mutuwo |