Mlaliki 9:17 - Buku Lopatulika17 Mau a anzeru achete amveka koposa kufuula kwa wolamulira mwa zitsiru. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Mau a anzeru achete amveka koposa kufuula kwa wolamulira mwa zitsiru. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mau a munthu wanzeru, olankhula mofatsa, ndi abwino kupambana kufuula kwa mfumu pa gulu la zitsiru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mawu oyankhula mofatsa a munthu wanzeru, anthu amawasamalira kwambiri kupambana kufuwula kwa mfumu ya zitsiru. Onani mutuwo |