Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 9:16 - Buku Lopatulika

16 Pamenepo ndinati, Nzeru ipambana mphamvu; koma anyoza nzeru ya wosauka, osamvera mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Pamenepo ndinati, Nzeru ipambana mphamvu; koma anyoza nzeru ya wosauka, osamvera mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ndiye ine ndikuti nzeru nzabwino ndithu kupambana mphamvu, ngakhale kuti anthu sazimvera nzeru za munthu wosauka, ndipo za mau ake salabadako nkomwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Choncho ine ndinati, “Nzeru ndi yopambana mphamvu.” Koma nzeru ya munthu wosauka imanyozedwa, ndipo palibe amene amalabadirako za mawu ake.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 9:16
13 Mawu Ofanana  

Chuma cha wolemera ndi mzinda wake wolimba; koma umphawi wao uononga osauka.


Wanzeru akwera pa mzinda wa olimba, nagwetsa mphamvu yake imene anaikhulupirira.


Mwamuna wanzeru ngwamphamvu; munthu wodziwa ankabe nalimba.


Ndine mwini uphungu ndi kudziwitsa; ndine luntha; ndili ndi mphamvu.


Chitsulo chikakhala chosathwa, ndipo ukaleka kunola, uzipambana kulimbikira; koma nzeru ipindulira pochenjeza.


Pakuti nzeru itchinjiriza monga ndalama zitchinjiriza; koma kudziwa kupambana, chifukwa nzeru isunga moyo wa eni ake.


Nzeru ilimbitsa wanzeru koposa akulu khumi akulamulira m'mzinda.


Nzeru ipambana zida za nkhondo; koma wochimwa mmodzi aononga zabwino zambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa