Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 9:14 - Buku Lopatulika

14 panali mzinda waung'ono muli anthu owerengeka; ndipo inadzako mfumu yaikulu, nawuzinga ndi nkhondo, nkumanga malinga aakulu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 panali mudzi waung'ono muli anthu owerengeka; ndipo inadzako mfumu yaikulu, niizinga ndi nkhondo, nimangapo malinga akulu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Panali mzinda waung'ono, m'mene munali anthu oŵerengeka. Tsono padafika mfumu yamphamvu kudzauthira nkhondo mzindawo, nkuuzinga ndi zithando zankhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Panali mzinda waungʼono umene unali ndi anthu owerengeka. Ndipo mfumu yamphamvu inabwera kudzawuthira nkhondo, inawuzungulira ndi kumanga mitumbira yankhondo.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 9:14
6 Mawu Ofanana  

Ndipo zitatha izi, Benihadadi mfumu ya Aramu anamemeza khamu lake lonse, nakwera, namangira misasa Samariya.


Ndaonanso nzeru pansi pano motero, ndipo inandionekera yaikulu;


Pakuti masiku adzakudzera, ndipo adani ako adzakuzingira linga, nadzakuzungulira iwe kwete, nadzakutsekereza ponsepo;


Koma mitengo yoidziwa inu kuti si ndiyo mitengo yazipatso, imeneyi muiononge ndi kuilikha; ndipo mzinda wochita nanu nkhondo muumangire machemba, mpaka mukaugonjetsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa