Mlaliki 9:13 - Buku Lopatulika13 Ndaonanso nzeru pansi pano motero, ndipo inandionekera yaikulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndaonanso nzeru pansi pano motero, ndipo inandionekera yaikulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pansi pano ndidaonanso chinthu china chokhudza nzeru, ndipo ine ndidachiwona kuti nchinthu chachikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ine ndinaonanso pansi pano chitsanzo ichi cha nzeru chimene chinandikhudza kwambiri: Onani mutuwo |