Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 9:13 - Buku Lopatulika

13 Ndaonanso nzeru pansi pano motero, ndipo inandionekera yaikulu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndaonanso nzeru pansi pano motero, ndipo inandionekera yaikulu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Pansi pano ndidaonanso chinthu china chokhudza nzeru, ndipo ine ndidachiwona kuti nchinthu chachikulu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Ine ndinaonanso pansi pano chitsanzo ichi cha nzeru chimene chinandikhudza kwambiri:

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 9:13
9 Mawu Ofanana  

Pomwepo mkaziyo anapita kwa anthu onse mwa nzeru yake. Ndipo iwo anadula mutu wa Sheba mwana wa Bikiri, nauponya kunja kwa Yowabu. Ndipo analiza lipenga, nabalalika kuchoka mumzindamo, munthu yense kunka ku hema wake. Ndipo Yowabu anabwerera kunka ku Yerusalemu kwa mfumu.


Pali choipa ndachiona kunja kuno chifalikira mwa anthu,


Ndaona zonsezi masiku anga achabe; pali wolungama angofa m'chilungamo chake, ndipo pali woipa angokhalabe ndi moyo m'kuipa kwake.


Nzeru ilimbitsa wanzeru koposa akulu khumi akulamulira m'mzinda.


Pompo ndinapereka mtima wanga kudziwa nzeru, ndi kupenya ntchito zichitidwa pansi pano; kuti anthu saona tulo konse ndi maso ao ngakhale usana ngakhale usiku;


Ndinabweranso ndi kuzindikira pansi pano kuti omwe athamanga msanga sapambana m'liwiro, ngakhale olimba sapambana m'nkhondo, ngakhale anzeru sapeza zakudya, ngakhale ozindikira bwino salemera, ngakhale odziwitsa sawakomera mtima; koma yense angoona zomgwera m'nthawi mwake.


Pakuti munthu sadziwatu mphindi yake; monga nsomba zigwidwa mu ukonde woipa, ndi mbalame zikodwa mumsampha, momwemo ana a anthu amagwidwa ndi nthawi ya tsoka, ngati msampha umene uwagwera modzidzimuka.


panali mzinda waung'ono muli anthu owerengeka; ndipo inadzako mfumu yaikulu, nawuzinga ndi nkhondo, nkumanga malinga aakulu;


Pamenepo Daniele anabweza mau a uphungu wanzeru kwa Ariyoki mkulu wa olindirira a mfumu, adatulukawo kukapha eni nzeru a ku Babiloni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa