Mlaliki 8:11 - Buku Lopatulika11 Popeza sambwezera choipa chake posachedwa atamtsutsa munthu, ana a anthu atsimikizadi mitima yao kuchita zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Popeza sambwezera choipa chake posachedwa atamtsutsa munthu, ana a anthu atsimikizadi mitima yao kuchita zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Oweruza akamachedwetsa chilango cha anthu opalamula, anthu ena amalimba mtima nkumafuna kuti ayambe kuchita zoipa nawonso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pamene chigamulo cha anthu opalamula mlandu chikuchedwa, mitima ya anthu imadzaza ndi malingaliro ochita zolakwa. Onani mutuwo |