Mlaliki 7:29 - Buku Lopatulika29 Taonani, ichi chokha ndachipeza kuti Mulungu analenga anthu oongoka mtima; koma iwowo afunafuna malongosoledwe a mitundumitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Taonani, ichi chokha ndachipeza kuti Mulungu analenga anthu oongoka mtima; koma iwowo afunafuna malongosoledwe a mitundumitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ndidapeza chokhachi chakuti Mulungu pomulenga munthu, adampatsa mtima wolungama, koma anthu amatsata njira zaozao zambirimbiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Chokhacho chimene ndinachipeza ndi ichi: Mulungu analenga munthu, anamupatsa mtima wolungama, koma anthu anatsatira njira zawozawo zambirimbiri.” Onani mutuwo |