Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 7:27 - Buku Lopatulika

27 Taonani, ichi ndachipeza, ati Mlalikiyo, m'kuphatikiza chinthu china ndi chinzake, ndikazindikire malongosoledwe ao;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Taonani, ichi ndachipeza, ati Mlalikiyo, m'kuphatikiza chinthu china ndi chinzake, ndikazindikire malongosoledwe ao;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Zimenezitu nzimene ndidazipeza pakusonkhanitsa izi ndi izi, kuti ndidziŵe m'mene zinthu zimakhalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Mlaliki akunena kuti, “Taonani, chimene ndinachipeza ndi ichi: “Kuwonjezera chinthu china pa china kuti ndidziwe mmene zinthu zimachitikira,

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 7:27
5 Mawu Ofanana  

Ine Mlaliki ndinali mfumu ya Israele mu Yerusalemu.


ndipo ndinapeza kanthu kowawa koposa imfa, ndiko mkazi amene ndiye msampha, mtima wake ukunga maukonde, manja ake ndiwo matangadza; yemwe Mulungu amuyesa wabwino adzapulumuka kwa iye; koma wochimwa adzagwidwa naye.


chomwe moyo wanga uchifuna chifunire, koma osachipezai ndi ichi, mwamuna mmodzi mwa chikwi ndinampezadi, koma mkazitu mwa onsewo sindinampeze.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa