Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 7:22 - Buku Lopatulika

22 pakuti kawirikawiritu mtima wako udziwa kuti nawenso unatemberera ena.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 pakuti kawirikawiritu mtima wako udziwa kuti nawenso unatemberera ena.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Mumtima mwako ukudziŵa kuti iweyonso udatukwanapo anthu ena.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 pakuti iwe ukudziwa mu mtima mwako kuti nthawi zambiri iwenso unatukwanapo ena.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 7:22
7 Mawu Ofanana  

Tsono mfumu inanenanso ndi Simei, Udziwa iwe choipa chonse mtima wako umadziwacho, chimene udachitira Davide atate wanga; chifukwa chake Yehova adzakubwezera choipa chako pamutu pako mwini.


Mau onsetu onenedwa usawalabadire; kuti usamve kapolo wako alikukutemberera;


Ndayesa zonsezi ndi nzeru; ndinati, Ndidzakhala wanzeru; koma inanditalikira.


Pakuti mumtima muchokera maganizo oipa, zakupha, zachigololo, zachiwerewere, zakuba, za umboni wonama, zamwano;


Timayamika Ambuye ndi Atate nalo; nalonso timatemberera anthu, okhala monga mwa mafanizidwe a Mulungu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa