Mlaliki 7:21 - Buku Lopatulika21 Mau onsetu onenedwa usawalabadire; kuti usamve kapolo wako alikukutemberera; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Mau onsetu onenedwa usawalabadire; kuti usamve kapolo wako alikukutemberera; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Usamasamala zonse zokamba anthu, mwinamwina udzamva wantchito wako akukutukwana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Usamamvetsere mawu onse amene anthu amayankhula, mwina udzamva wantchito wako akukutukwana, Onani mutuwo |