Mlaliki 7:20 - Buku Lopatulika20 Pakuti kulibe wolungama pansi pano amene achita zabwino osachimwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pakuti kulibe wolungama pansi pano amene achita zabwino osachimwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ndithudi, pa dziko lapansi palibe munthu amene amachita zabwino zokhazokha osachimwa konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Palibe munthu wolungama pa dziko lapansi amene amachita zabwino zokhazokha ndipo sachimwa. Onani mutuwo |