Mlaliki 6:11 - Buku Lopatulika11 Pokhala zinthu zambiri zingochulukitsa zachabe, kodi anthu aona phindu lanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pokhala zinthu zambiri zingochulukitsa zachabe, kodi anthu aona phindu lanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mau akachuluka, zopandapake zimachulukanso. Nanga munthu apindulapo chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mawu akachuluka zopandapake zimachulukanso, nanga munthu zimamupindulira chiyani? Onani mutuwo |