Mlaliki 5:9 - Buku Lopatulika9 Phindutu la dziko lipindulira onse; ngakhale mfumu munda umthandiza; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Phindutu la dziko lipindulira onse; ngakhale mfumu munda umthandiza; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Alimi onse amatengako dzinthu dzam'minda, koma ndi mfumu yokha imene imaona phindu lake la mindayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Anthu onse amatengako zokolola za mʼminda: koma ndi mfumu yokha imene imapeza phindu la mindayi. Onani mutuwo |