Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 5:9 - Buku Lopatulika

9 Phindutu la dziko lipindulira onse; ngakhale mfumu munda umthandiza;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Phindutu la dziko lipindulira onse; ngakhale mfumu munda umthandiza;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Alimi onse amatengako dzinthu dzam'minda, koma ndi mfumu yokha imene imaona phindu lake la mindayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Anthu onse amatengako zokolola za mʼminda: koma ndi mfumu yokha imene imapeza phindu la mindayi.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 5:9
15 Mawu Ofanana  

Kunena za kumwamba, kumwamba ndiko kwa Yehova; koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu.


M'kulima kwa osauka muli zakudya zambiri; koma zinazo zimaonongeka posowa chiweruzo.


Wolima munda wake zakudya zidzamkwanira; koma wotsata anthu opanda pake umphawi udzamkwanira.


Pali mmodzi palibe wachiwiri; inde, alibe mwana ngakhale mbale; koma ntchito yake yonse ilibe chitsiriziro, ngakhale diso lake silikhuta chuma. Samati, Ndigwira ntchito ndi kumana moyo wanga zabwino chifukwa cha yani? Ichinso ndi chabe, inde, vuto lalikulu.


Wokonda siliva sadzakhuta siliva; ngakhale wokonda chuma sadzakhuta phindu; ichinso ndi chabe.


Ukaona anthu alikutsendereza aumphawi, ndi kuchotsa chilungamo ndi chiweruzo mwachiwawa pa dera lina la dziko, usazizwepo; pakuti mkulu wopambana asamalira; ndipo alipo akulu ena oposa amenewo.


Ntchito zake zonse munthu angogwirira m'kamwa mwake, koma mtima wake sukhuta.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa