Mlaliki 5:14 - Buku Lopatulika14 koma chumacho chionongeka pomgwera tsoka; ndipo akabala mwana, m'dzanja lake mulibe kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma chumacho chionongeka pomgwera tsoka; ndipo akabala mwana, m'dzanja lake mulibe kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndiye chuma chimenecho chikamwazika moipa, munthuyo nkukhala ndi ana, amachita kusoŵa choŵapatsa ana akewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 kapena chuma chowonongedwa pa nthawi yatsoka, kotero kuti pamene wabereka mwana alibe kanthu koti amusiyire. Onani mutuwo |