Mlaliki 4:15 - Buku Lopatulika15 Ndinapenyera anthu onse amoyo akuyenda kunja kuno, kuti anali ndi mwana, wachiwiri, amene adzalowa m'malo mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndinapenyera anthu onse amoyo akuyenda kunja kuno, kuti anali ndi mwana, wachiwiri, amene adzalowa m'malo mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndinkaganiza za anthu onse amene amakhala pansi pano, ndipo ndidazindikira kuti pakati paopo panali mnyamata uja amene anali wodzatenga malo a mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndipo ndinaona kuti iwo onse amene anakhala ndi moyo ndi kuyenda pansi pano anatsatira wachinyamatayo, amene anatenga malo a mfumu. Onani mutuwo |