Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 2:25 - Buku Lopatulika

25 Pakuti ndani angadye ndi kufulumirako, koposa ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Pakuti ndani angadye ndi kufulumirako, koposa ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Nanga popanda Iye ndani angathe kudya, ndani angathe kusangalala?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 pakuti popanda Iye, ndani angadye ndi kupeza chisangalalo?

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 2:25
4 Mawu Ofanana  

Kodi si chabwino kuti munthu adye namwe, naonetse moyo wake zabwino m'ntchito yake? Ichinso ndinachizindikira kuti chichokera kudzanja la Mulungu.


Pakuti yemwe Mulungu amuyesa wabwino ampatsa nzeru ndi chidziwitso ndi chimwemwe; koma wochimwa amlawitsa vuto la kusonkhanitsa ndi kukundika, kuti aperekere yemwe Mulungu amuyesa wabwino. Ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa