Mlaliki 2:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo ndinatembenuka ndi kukhululuka za ntchito zanga zonse ndasauka nazo kunja kuno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo ndinatembenuka ndi kukhululuka za ntchito zanga zonse ndasauka nazo kunja kuno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Motero ndidayamba kutaya mtima chifukwa cha ntchito zonse zimene ndidazigwira movutikira pansi pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Motero ndinayamba kutaya mtima chifukwa cha ntchito zonse zimene ndinazivutikira pansi pano. Onani mutuwo |