Mlaliki 12:7 - Buku Lopatulika7 fumbi ndi kubwera pansi pomwe linali kale, mzimu ndi kubwera kwa Mulungu amene anaupereka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 fumbi ndi kubwera pansi pomwe linali kale, mzimu ndi kubwera kwa Mulungu amene anaupereka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pamenepo thupi lidzabwerera ku dothi monga m'mene lidaaliri, ndipo mzimu udzabwerera kwa Mulungu amene adaupereka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iyi ndi nthawi imene thupi lidzabwerera ku dothi, kumene linachokera, mzimu udzabwerera kwa Mulungu amene anawupereka. Onani mutuwo |